Professional Documents
Culture Documents
MNZAKE WA MULUNGU!
NKHANI ZA MKATI
PHUNZILO
Mmene Mungadziwile
Cipembedzo Coona
9
10
11
12
13
14
15
16
17
18
2009
Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
Na Imwe Mungakhale Mnzake wa Mulungu!
Ofalitsa:
Printed by Watch Tower Bible and Tract Society of South Africa NPC
1 Robert Broom Drive East, Rangeview, Krugersdorp, 1739, R.S.A.
Kabuku kano kanapulintiwa mu June 2014
Colinga ca kabuku kano ni kuthandiza panchito yophunzitsa Baibo
imene icitika padziko lonse. Zopeleka zodzifunila ni zimene
zimathandiza kuti nchito imeneyi ipite patsogolo.
Mu kabuku kano talembamo Cinyanja camasiku ano cimene
P H U N Z I LO 1
P H U N Z I LO 2
P H U N Z I LO 3
Koma kudziwa munthu kumatenga nthawi. Baibo imakamba kuti ni cinthu canzelu kupatula nthawi ya kuphunzila za Yehova.Aefeso 5:
15, 16.
Anzake a Mulungu amacita zimene zimamukondweletsa. Mwacitsanzo, tiyeni tikambe za
anzanu. Ngati mumawavuta na kucita zinthu zimene samafuna, kodi angapitilize kukhala anzanu? Kutalitali! Ni cimodzimodzi na Mulungu.
Ngati imwe mufuna kukhala mnzake, mufunikila kucita zimene iye amafuna.Yohane 4:24.
Kodi zipembedzo zonse zingakuthandizeni kukhala mnzake wa Mulungu? Iyai.
Yesu, amene ni mnzake wa Mulungu wapa
mtima, anaphunzitsa ponena za njila ziwili.
Ina niikulu ndipo ili ndi anthu ambili oyendamo. Njila imeneyo imapeleka ku cionongeko. Koma njila ina niingono ndipo anthu
oyendamo ni ocepa. Njila imeneyi imapeleka
ku moyo wosatha. Conco, ngati mufuna kukhala mnzake wa Mulungu, mufunikila kuphunzila mmene mungamulambilile mu njila yoyenela.Mateyu 7:13, 14.
5
P H U N Z I LO 4
Mungaphunzile za Mulungu mwa kuwelenga Baibo. Kale kwambili, Mulungu anasankha anthu ena kuti alembe maganizo ake.
Zimene analemba zimapanga buku lochedwa
kuti Baibo. Masiku ano timaphunzila za Mu
lungu mwa kuwelenga Baibo. Baibo imachedwanso kuti Mau a Mulungu cifukwa muli
mau a Yehova, kapena kuti uthenga wake. Tingakhulupilile zimene Baibo imakamba cifukwa Yehova sanganame. Mulungu sakhoza
kunama. (Ahebri 6:18) Mau a Mulungu ndiye
coonadi.Yohane 17:17.
monga dzuwa. Zimatiphunzitsanso kuti Yehova ali na nzelu. Takamba conco cifukwa sembe
P H U N Z I LO 5
P H U N Z I LO 6
10
11
P H U N Z I LO 7
KUTENGAPO PHUNZILO PA
ZIMENE ZINACITIKA KUMBUYO
Yehova sadzalola kuti anthu oipa akakhalemo mu Paladaiso cifukwa angaiwononge.
Anzake cabe a Mulungu ni amene adzakhalamo.
Nanga anthu oipa cidzawacitikila ni ciyani? Kuti
Nowa na Banja lake anapanga cingalawa. Cigumula cikalibe kubwela, Nowa anacenjeza
anthu, koma iwo sanamumvele. Iwo anapitiliza kucita vinthu voipa. Pamene Nowa anatsili
za kupanga cingalawa, analowetsamo vinyama.
Ndiyeno, iye na banja lake anangena mu cingalawa. Pambuyo pake, Yehova anabweletsa cimvula cikulu. Cimvula cimeneco cinagwa kwa masiku 40 usana na usiku. Ndipo madzi amenewo
anaculuka na kudzala padziko lonse lapansi.
Genesis 7:7-12.
12
P H U N Z I LO 8
mucite. Satana na viwanda vake amazondana na Yehova. Iwo ni adani a Mulungu, ndipo amafuna kuti na imwe mukhale mdani wa Mulungu. Conco, muyenela kusankha
amene mufuna kukondweletsaSatana kapena Yehova. Ngati mufuna moyo wosatha,
muyenela kucita zimene Mulungu amafuna. Satana ali na njila zambili zonamilamo anthu. Iye amapusitsa anthu ambili.Cibvumbulutso 12:9.
14
P H U N Z I LO 9
P H U N Z I LO 10
16
P H U N Z I LO 11
Satana na viwanda vake safuna kuti imwe muzitumikila Mulungu. Iwo amafuna kuti acotse munthu aliyense ku mbali ya Mulungu ngati
angakwanitse. Kodi amayesa kucita zimenezi kupitila mu njila za bwanji? Imodzi mwa njila zimenezo ni cipembedzo conama. (2 Akorinto 11:1315) Cipembedzo ciliconse cimene cimaphunzitsa
zimene sizicokela mu Baibo ni conama. Cipembedzo conama cili monga ndalama yabodzangakhale kuti ingaoneke monga ni yazoona, imakhala ilibe nchito. Ingakubweletseleni mavuto akulu.
Mabodza a cipembedzo sangakondweletse Yehova, Mulungu wa coonadi. Pamene Yesu anali padziko lapansi, panali anthu ena acipembedzo amene anafuna kumupha. Anali kuona kuti
cipembedzo cawo ndiye cinali coona. Iwo anakamba kuti: Tili naye tate mmodzi ndiye Mulungu. Kodi Yesu anavomeleza zimenezo? Kutalitali! Koma iye anawauza kuti: Inu muli ocokela
mwa atate wanu Mdyelekezi. (Yohane 8:41, 44)
Anthu ambili masiku ano amaganiza kuti amalambila Mulungu, koma kwenikweni amatumikila
P H U N Z I LO 12
Satana na viwanda vake amapangitsa anthu kuganiza kuti mizimu ya anthu amene anafa ili na
moyo. Amakamba kuti mizimu imeneyo ni imene imadwalitsa anthu na kubweletsa mavuto ena.
Nthawi zina Satana amanama anthu kupitila
mmaloto na masomphenya oona vinthu. Yehova
amawazonda anthu amene amayesa kukamba na
anthu amene anafa.Deuteronomo 18:10-12.
P H U N Z I LO 13
P H U N Z I LO 14
23
P H U N Z I LO 15
24
25
P H U N Z I LO 16
Muziwelenga Mau a Mulungu, Baibo. Lemba lililonse adaliuzila Mulungu, ndipo lipindulitsa pa ciphunzitso, citsutsano, cikonzelo,
cilangizo ca mcilungamo.2 Timoteo 3:16.
Muziphunzitsa ena za Mulungu. Cifukwa
cake mukani, phunzitsani anthu a mitundu
yonse, . . . asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulilani inu.Mateyu 28:19, 20.
26
Khalani mnzawo wa aja amene ni anzake a Mulungu. Ukayenda ndi anzelu udzakhala wanzelu.Miyambo 13:20.
Muzipezeka kumisonkhano ku Nyumba
ya Ufumu. Tiyeni tiganizilane wina ndi
mnzake, kuti tilimbikitsane pa cikondi ndi
nchito zabwino.Ahebri 10:24, NW.
Muzithandiza panchito ya Ufumu na zopeleka zanu. Yense acite monga atsimikiza
mtima, si mwa cisoni kapena mokakamiza,
pakuti Mulungu akonda opeleka mokondwelela.2 Akorinto 9:7.
27
P H U N Z I LO 17
29
P H U N Z I LO 18
31
Kodi mufuna kudziwa zambili?
gf-CIN
140704