You are on page 1of 1

KODI MUKUDZIWA ZA NJIRA ZOLERERA

ZOMWE MUNGAGWIRITSE NTCHITO?


Alangizi anu a zakulera akhoza kukuthandizani. Chonde funsanu!

Mapiritsi
Jakisoni Kondomu Lupu
a mphamvu ziwiri
• Ndi yodalirika ndiponso nkosavuta mayi kutenga • Ndi yodalilika komanso yotetezeka. • Imathandiza kupewa mimba ndi matenda ena • Kapulasitiki kakang'ono kamene kamaikidwa
mimba ngati atasiya kugwiritsa ntchito. opatsilana pogonana kuphatikizapo EDZI, m’chibelekelo cha amayi.
• Mayi amabayitsa kamodzi pa miyezi itatu iliyonse
• Imwani pilitsi limodzi tsiku lili lonse ndi kuyamba (masabata khumi ndi atatu) ndi DPMA, miyezi iwiri mukagwiritsa ntchito moyenera nthawi zonse. • Ndi yodalilika kwambiri imakhala nthawi yaitali ndipo
paketi ya tsopano panthawi yake kuti mapilitsiwo iliyonse ndi NET-EN. Mayi akhoza kuchedwerapo mayi amatenga mimba mosavuta akachotsa. Mayi atha
agwire ntchito bwino.
• Kuti atetezedwe ku matenda opatsirana pogonana kukhala nayo mpaka zaka khumi ndi ziwiri.
kudzabayitsa jakisoni ndi masabata anayi ndi DPMA
kapena masabata awiri ndi NET-EN. kuphatikiza Edzi mabanja ena amagwiritsa ntchito
• Kusamba mosayembekezera kapena modontheza makondomu pambali pa njira zina zolelera. • Lupu ikhonza kuikidwa mayi akangobereka kumene,
kukhoza kuchitika makamaka mu miyezi • Ndizothekera kukalandira jakisoni kunja kwa ngakhalenso nthawi yina ili yonse komanso akhonza
yoyambirira. Izi sizoopysa. Msambo umayamba chipatala. • Ndi yosavuta kugwilitsa ntchito ngati osatero malingana ndi njira yake ya lupu.
kuchepa komanso umachitika mu nthawi yake mwaphunzitsidwa.
pakapita miyezi ingapo. • Kusamba modukizadukiza kapena kudonthetsa • Mayi akhoza kumva kupweteka poyika Mayi akhonza
kumakhalapo miyezi ingapo yoyambirira, kenako • Ndi yodalilika mukagwilitsa ntchito moyenela kusamba kwambiri komanso kutenga nthawi yaitali
• Amayi ena amamva kupweteka kwa mutu, ena mayi amasiyirathu kusamba. Pang’ono ndi pang’ono akusamba, makamaka poyamba, Ndi njira yimeneyi mai
amaneneperako, ena amamva cham'mimba nthawi zonse. Komano anthu sakonda kuigwirisa
mayi amanenepa, amamva kupweteka mutu. Koma sataaya magazi ambiri ndipo imathandiza ku matenda
makamaka mu miyezi yoyambirira. Izi zimasiya siyodetsa nkhawa. ntchito nthawi zambiri. ochepa magazi.
pakapita kanthawi.
• Ndi yachinsinsi Anthu ena sangadziwe kuti mayi • Anthu ena amakana kondomu chifukwa • Zovuta zodetsa nkhawa sizichitikachitika Ngati mayi ali
• Ndi yabwino pafupifupi kwa mayi aliyense. Zovuta akugwilitsa ntchito njira imeneyi. imawasokoneza pogonana, imachepetsa kukoma ndi matenda opatsilana pogonana nthawi imene lupuyo
zodetsa nkhawa sizichitikachitika. kwa kugonana ndiponso imawachititsa manyazi. imaikidwa ndikwapafupi kukhala ndi matenda a
• Njirayi itha kugwiritsidwa ntchito ndi mai wa mchibelekelo.
• Ikhoza kugwiritsidwa ntchito ndi mayi wamsinkhu msinkhu wina uli onse, kaya anabelekapo kapena
wina uliwonse kaya anaberekapo kale kapena ayi. ayi. • Itha kutuluka kapena kugwa payokha makamaka
• Imathandiza kuchepetsa cham’mimba pamene mayi • Mayi akasiya kugwiritsa ntchito njirayi atha Njira Yapamkono masiku oyambilira.
akusamba, kutaya magazi ambiri posamba, kutenganso mimba, koma amayi ena • Mayi amatenga mimba mosavuta akachotsa lupu.
kuperewera kwa magazi ndi zovuta zina. amachedwelapo. Pakapita miyezi itatu, atalandira
jakisoni pakhoza kupitanso miyezi ingapo.
• Timachubu ta pulasitiki timene timaikidwa pa
• Njirayi njodalilika pamene mayi akuyamwitsa, nkono wa mayi. Palibenso china chochitika akaika
Kutseka Kwa Amayi kuyambira masabata asanu ndi imodzi mwana
atabadwa.
timachubuto pamkono.

• Jakisoni wa mwezi uliwonse akhoza kupezeka. Ndi


• Mayi sangatenge mimba kwa zaka zitatu mpaka Njira Yolerera Poamwitsa
• Njirayi ndi ya muyaya. Ndi ya amayi okhawo amene
jakisoni wa Cyclo-fem msambo wa mwezi ndi mwezi
zisanu ndi ziwiri malingana ndi mtundu wa njira
yapankono. Mkaka Wa M’mawere
umakhala wocheperapo komanso wamasiku
atsimikiza kuti sakufuna kudzaberekanso ana.
ochepa. Mayi atha kusamba modonthetsa kapena • Njirayi itha kugwiritsidwa ntchito ndi mayi aliyense
Kotero ganizani mozama musanasankhe njirayi. ngakhale amene sanabelekepo. • Ndi njira yolerera poyamwitsa mwana mkaka
mosayembekezera.
• Ndi njira yodalirika kwambiri (koma osati • Njira ya pamkono itha kuchotsedwa ndi amene wam'mawere mwakathithi mpakana atakwanitsa miyezi
kwathunthu). anaphunzitsidwa za chipatala nthawi yina yiri yonse isanu ndi umodzi.
• Amayi amayezedwa thupi lonse ndipo adokotala Zikaterono mayi atha kutenga mimba. • Mayi amagwiritsa ntchito njirayi ngati:
amapanga opaleshoni yomwe ili yosaopsa ndiponso • Kusamba mosayembekezera kapena modonthetsa - Mwanayo amamuyamwitsa mwakathithi usana ndi
yosavuta. Mayi sampatsa mankhwala ogonetsa pa Mapilitsi kumakhalapo, koma nthawi zambiri msambo usiku ndipo sapatsidwa chakudya kapena madzi
nthawi ya opaleshoni. Amabayidwa jakisoni woletsa
ululu. a mphamvu imodzi umasiyiratu. Izisizodetsa nkhawa. - Mayiyo sanayambe kusamba kwa mwezi ndi mwezi
- Mwanayo ndiosafika mwiyezi isanu ndi umodzi.
• Njirayi ilibe vuto kwa mayi amene akuyamwitsa
• Amamva kupweteka komanso kutupa kwa masiku kuyambila masabata asa asanu ndi imodzi mwana • Asanasiyiletu kugwiritsa ntchito njira yoyamwitsayi,
ochepa. Zovuta zodetsa nkhawa sizichitikachitika. • Ndi yabwino kwa mayi woyamwits amene akufuna atabadwa. mayi akonzekere kugwiritsa ntchito njira yina yolerera.
• Zotsatira zovuta sizikhala nthawi yayitali. Siichepetsa mapilisi kuyambira sabata yachisanu ndi chimodzi
chilakolako chofuna kugonana. atabereka.

• Njira iyi ikhonza kupangidwa mayi atangobereka • Ndi njira yodalilika pamene mayi akuyamwitsa
kumene, ngakhalenso nthawi ina ili yonse. koma akhoza kutenga mimba mosavuta akasiya
kumwa mapilitsi.

Kutseka Abambo
• Mayi amwe pilitsi limodzi tsiku lili lonse kuti Njira Yachilengedwe
atetezedwe mokwanira.
YODZIWA NTHAWI YOTENGELA MIMBA Njira yolerera ya pa pangozi
(Vasekitome) • Ngati mayi sakuyamwitsa, kudonthetsa kapena
• Awa ndi mapilitsi amene amathandiza
kusamba mosayembekezera kumachitika Izi
sizodetsa nkhawa. kupewa mimba ngati mayi angalandire
• Njirayi ndi ya muyaya Ndi ya abambo okhawo amene • Mayi amaphunzitsidwa kudziwa nthawi yomwe chithandizochi pasanapite masiku – asanu
sakufuna kudzaberekanso ana ganizani mozama angatenge mimba. chigonaniraneni ndi mwamuna
musanasankhe njirayi.
• Gwiritsani ntchito njira ina yolerera mpaka patatha
Chifunda mtima • Panthawi imeneyi banja lipewe kugonana kapena
ligwilitse ntchito kondomu.
mosadziteteza kapena kusagwiritsa ntchito
bwino njira yolerera.
miyezi itatu kuchokera tsiku limene opaleshoni ndi umuna • Ndiyodalilika mukatsatira moyenera Koma nthawi
inachitika. • Ndi njira yodalilika kwa mayi wina ali yense.
zina siyodalilika.
• Ndi njira yodalirika kwambiri pakapita miyezi itatu. • Mayi amaika chifunda mtima mkati mwa maliseche • Siimasokoneza mimba kapena kubweretsa
(koma osati kwathunthu) • Mwamuna ndi mkazi ayenera kugwirizana
ake nthawi zonse asanagonane. Akhoza kupanga pogwiritsa ntchito njirayi. zovuta kwa mwana woyembekezeredwayo
• Opaleshoni yake ndi yosavuta, yotetezeka komanso zimenezi nthawi isanakwane. ngati mayiyo ali ndi mimba kale.
yochitika mwabwino Imachitika mu mphindi zochepa • Ilibe zoopsa zina zili zonse kuthupi la munthu.
• Ndi yodalilika mukaigwiritsa ntchito bwino. • Njira zolelera ndizabwino kwambiri ngati
abambo samva kuwawa. • Njira zina zitha kukhala zovuta kugwiritsa ntchito
• Mayi ayenera kuyezedwa ziwalo za mkati kuti apeze pamene mayi wadwala malungo, kapena matenda a mwazitsatira. Chonde pezani njira yoti
• Amamva kupweteka komanso kutupa kwa masiku chifunda mtima cha saizi yabwino.
ochepa. Abambo ochepa amamvabe ululu kwa kumaliseche, atangobeleka kumene kapena mutsatire.
nthawi yayitali. • Amadwaladwala matenda a mchikozozo. akuyamwitsa.

• Njirayi siichepetsa chilakolako chofuna kugonana.

Njira Zina Sizoyenekera Kwa Amayi Ena Malingana Ndi M’mene Umoyo Wawo Ulili

Mmene umovo ulili Njira zosawayenera


Muyezo Wa Kudalirika Kwa Njira Zolelera
Amasuta komanso ali ndi zaka makumi atatu ndi Mapilitsi a mphamvu ziwiri Jakisoni wa mwezi ndi mwezi
zisanu kapena kuposera pamenepa. ngati mayi amasuta kwambiri.
Zodalirika kwambiri Kodi mungapange bwanji kuti njira
Ali ndi vuto lothamanga kwa Magazi. Jakisoni wa mwezi ndi mwezi. Ngati akuthamanga Mwa amayi 100 aliwonse mayi mmodzi yekha yanu ikhale yodalilika?
kwambiri magazi jakisoni pa miyezi iwiri ndi itatu. akhoza kutenga mimba pa chaka chimodzi
Ngati mayi akuyamwitsa mwakathithi mwana Jakisoni wa mwezi ndi mwezi. Nolopulant, Lupu, kutseka kwa amayi:
asanakwane miyezi isanu ndi umodzi. Palibe zambiri zofuna kuchita komanso
Ngati mayi akuyamwitsa masabata asanu ndi Jakisoni wa miyezi iwiri komanso itatu. nolopulanti ndi
kukumbukira.
imodzi chibadwireni cha Mwana. mapilitsi a mphamvu imodzi.
Nolopulanti Lupu Kutseka kwa Kutseka kwa Kutseka kwa abambo: Gwiritsani ntchito njira
Masiku makumi awiri ndi mphambu imodzi Mapilitsi a mphamvu ziwiri Jakisoni wa mwezi ndi mwezi.
mayi bamboo ina yolerera kwa miyezi itatu.
(21) chibadwireni cha mwana komanso ngati Mapilisi komanso jakisoni ngosabvomerezeka kwa masabata
sakuyamwitsa. asanu ndi imidzi mai atabereka pokhapokha pali pali Jakisoni: Kabayitseni pa nthawi yake.
chifukwa chokwanira kuti magazi angaundane. Kuundana
kwa magazi kumakulaa kwambiri miyezi yoyambilira maai Lactational Amenorrhea Method: Yamwitsani
atabereka Mudikire masabaata asanu ndi imodzi kuti
chiberekero chikhale m’malo mwake. usana ndi usiku mwakathithi.
Mapilitsi: Imwani tsiku lililonse.
Matenda monga a mtima, a m'misempha ya magazi, Mapilitsi onse. Jakisoni Nolopulanti Funsani zambiri kwa Jakisoni Njira Mapilitsi Ling’i Lupu
a mchiwindi komanso khansa ya m'mawere. alangizi anu azakulera. yoyamwitsa Zigamba ndi ling’i: iikidwe pa malo ake, sinthani
Mutu wa ching'alang'ala komanso ngati mayiyo ali
mwakathithi mu nthawie yake.
Mapilitsi a mphamvu ziwiri, jakisoni wa mwezi ndi mwezi.
ndi zaka makumi atatu ndi mphambu zisanu (35)
kapena kuposerapo.
Funsani zambiri kwa alangizi anu azakulera.
Kondomu, chifunda mtima: Gwiritsani ntchito
Matenda a kowala pa diso la mayi mu zaka ziri zonse. Mapilitsi a mphamvu ziwiri, jakisoni wa mwezi ndi mwezi. moyenera nthawi zones mukugonana.
Funsani zambiri kwa alangizi anu azakulera.
Njira yachilengedwe: Peweni kugonana kapena
Mapilitsi a mphamvu ziwiri Funsani zambiri kwa alangizi anu
Matenda a m'ndulu.
azakulera.
gwilitsani ntchito kondomu Njira yogonana
Makondomu Chifunda Makondomu Njira yachilengedwe masiku amene mkazi sangatenge mimba ikhoza
Matenda ena a m'ziwalo zoberekera za amayi. Lupu. a abambo mtima a amayi
kukhala yapafupi kugwiritsa ntchito.
Matenda opatsirana pogonana kuphatikizapo EDZI. Gwiritsani ntchito makondomu ngakhale mukugwiritsa ntchito Kuthira, umuna: Gwiritsani ntchito moyenera
njira ina yolerera.
nthawi zonse mukugonana.
Amayi amene ali ndi HIV kapena EDZI ndipo akulandira
chithandizo akhoza kugwiritsa ntchito njira yolerera
iliyonse (Kuphatikizapo lupukapena mai amene ali ndi Zodalirika mocheperapo Kuthira Umuna
EDZI ngati akulandira mankhwala ndipo alibe vuto.
Mwa amayi 100 aliwonse amayi
30 akhoza kutenga mimba pa chaka chimodzi
Mai ali ndi mimba. Palibe njira yiri yonse ikufunika.

Kwa opereka njira zakulera Funsani kwa oyang; anira kuti mulandire uphungu woyenera
Kuti mudziwe zambiri za njira zolerera, alangizi za zakulera akhoza kuyan’ana mu bukhu la zakulera: A Global Handbook for Providers.
Alangizi a zakuthanzi akhoza kupeza bukhuli ndi makope ena a chosindikiza ichi kuchokera ku K4JHealth, Johns Hopkins Bloomberg School of Public
Health/Center for Communication Programs, 111 Market Place, Suite 310, Baltimore, Maryland 21202, U S A; email orders@huccp.org
Chipepalachi chalowa m’malo a chosindikiza cha kale Chosindikizachi chatheka ndi chithandizo chochokera ku Unites States Agency for International
Development, Global, GH/PRHPEC, pa mgwirizano wa Chithandizo cha nambala GPO-A- 00-08-00006-00. Chosinthidwa 2010 Johns Hopkins Bloomberg School
of Public Health Center for Communication Programs.

You might also like