Professional Documents
Culture Documents
Malangizo:
malangizo
Yankhani mafunso awa mumalo omwe adulidwa nzeru kunsi kwa mfunso lina lililonse
Tsiku lina Tadala amapita ku sukulu. Panjira adakumana ndi bamboo wina yemwe adanyamula
thumba la Makala logulitsa. Tadala adali ataphunzira ku sukulu kufunika kosamala zithu
zachilengedwe.
Tadala adalingalira zochita kuti mchitidwe wowotcha Makala uthe. Adakumbukira zomwe
akuphunzitsi ake ankanena kuti mitengo ikatha m’dziko, mvula imavuta komanso makhwala
azitsamba amasowa.
13. Tchulani zithu zomwe mungachite pochepetsa mchitidwe odula mitengo (5 malikisi)
14. Kodi mitengo ikatha zimabweretsa mavuto anji (tchulani fundo ziwiri kuchokera mu nkhaniyi) (5
malikisi)
15. Tchulani zithu ziwiri zogwiritsa ntchito pakhomo (5 malikisi)
16. Jambulani chikwangwani cha pa mseu chimodzi (20 malikisi)
17. Kodi owoloka mseu timayenera kuti titani (5 malikisi)