Professional Documents
Culture Documents
20200520b Gospel in Practice
20200520b Gospel in Practice
GOSPEL IN PRACTICE
Mbali Zonsezonse
1Thess 5:23 Ndipo Mulungu wa mtendere
yekha ayeretse inu konse konse; ndipo mzimu
wanu ndi moyo wanu ndi thupi lanu
zisungidwe zamphumphu, zopanda chilema pa
kudza kwake kwa Ambuye wathu Yesu Khristu.
(1Th 5:23 And the very God of peace sanctify
you wholly; and I pray God your whole spirit
and soul and body be preserved blameless unto
the coming of our Lord Jesus Christ).
Yesu Anagonjetsa
• Rom 8:3 For what the law could not do, in that it was
weak through the flesh, God sending his own Son in the
likeness of sinful flesh, and for sin, condemned sin in the
flesh:
• Rom 8:4 That the righteousness of the law might be
fulfilled in us, who walk not after the flesh, but after the
Spirit.
• (Rom 8:3 Pakuti chimene chilamulo sichidathe kuchita
popeza chidafoka mwa thupi, Mulungu adatumiza Mwana
wake wa Iye yekha m’chifanizo cha thupi la uchimo, ndi
chifukwa cha uchimo, natsutsa uchimo m’thupi:
• Rom 8:4 Kuti chilungamo cha chilamulo chikakwaniridwe
mwa ife, amene sitiyendayenda monga mwa thupi, koma
monga mwa mzimu.)
Chosowa cha Dziko
• Rom 8:19 Pakuti chiyembekezetso cha cholengedwa
chilindira kuwonekera kwa ana a Mulungu.
• Rom 8:20 Pakuti cholengedwacho chigonjetsedwa ku
utsiru, chosafuna mwini, koma chifukwa cha Iye amene
adachigonjetsa, mchiyembekezo.
• Rom 8:21 Pakuti cholengedwacho chidzamasulidwa ku
ukapolo wachibvundi, ndi kulowa ufulu wa ulemerero wa
ana a Mulungu.
• Rom 8:22 Pakuti tidziwa kuti cholengedwa chonse
chibuwula, ndi kugwidwa m’zowawa pamodzi kufikira
tsopano.
• Rom 8:23 Ndipo sichotero, koma ife tomwe; tiri nazo
zowundukula za Mzimu, inde ifenso tibuwula m’kati
mwathu, ndi kulindilira umwana wathu, ndiwo
chiwomboledwe cha thupi lathu.
That perfection of character which the Lord requires is the fitting
up of the whole being as a temple for the indwelling of the Holy
Spirit. God will accept of nothing less than the service of the entire
human organism. It is not enough to bring into action certain parts of
the living machinery. All parts must work in perfect harmony, or the
service will be deficient. It is thus that man is qualified to cooperate
with God in representing Christ to the world. Thus God desires to
prepare a people to stand before Him pure and holy, that He may
introduce them into the society of heavenly angels. {OFC 108.2}
Mar 12:29 Ndipo Yesu adamuyankha iye, Kuti lamulo loyamba la onse
ndi ili, Mvera, Israyeli; Ambuye Mulungu wathu ndiye m’modzi.
Mar 12:30 Ndipo uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wako
wonse (spiritual), ndi moyo wako wonse (whole person), ndi nzeru
zako zonse (mental), ndi mphamvu yako yonse (physical): Ili ndi lamulo
loyamba.
Mar 12:31 Ndipo lachiwiri ndi ili, uzikonda mzako monga uzikonda iwe
mwini (social). Palibe lamulo lina loposa awa.
Cholinga cha Maphunziro Oona
To restore in man the image of his Maker, to bring him back to the perfection
in which he was created, to promote the development of body, mind, and
soul, that the divine purpose in his creation might be realized--this was to be
the work of redemption. This is the object of education, the great object of
life. {Ed 15.2}
The first and great commandment is, "Thou shalt love the Lord thy God with
all thy heart, and with all thy soul, and with all thy strength, and with all thy
mind." Luke 10:27. To love Him, the infinite, the omniscient One, with the
whole strength, and mind, and heart, means the highest development of
every power. It means that in the whole being--the body, the mind, as well as
the soul--the image of God is to be restored. {Ed 16.1}
Like the first is the second commandment--"Thou shalt love thy neighbor as
thyself." Matthew 22:39. The law of love calls for the devotion of body, mind,
and soul to the service of God and our fellow men. And this service, while
making us a blessing to others, brings the greatest blessing to ourselves.
Unselfishness underlies all true development. Through unselfish service we
receive the highest culture of every faculty. {Ed 16.2}
MOYO NDIWO KUUNIKA KWA DZIKO
• The apostle Paul, in his labors at Ephesus, was given special tokens of divine
favor. The power of God accompanied his efforts, and many were healed of
physical maladies. "God wrought special miracles by the hands of Paul: so that
from his body were brought unto the sick handkerchiefs or aprons, and the
diseases departed from them, and the evil spirits went out of them." These
manifestations of supernatural power were far more potent than had ever
before been witnessed in Ephesus, and were of such a character that they could
not be imitated by the skill of the juggler or the enchantments of the sorcerer.
As these miracles were wrought in the name of Jesus of Nazareth, the people
had opportunity to see that the God of heaven was more powerful than the
magicians who were worshipers of the goddess Diana. Thus the Lord exalted His
servant, even before the idolaters themselves, immeasurably above the most
powerful and favored of the magicians. {AA 286.4}
Self-Supporting Professional Work
• Act 18:1 Zitapita zinthu izi, Paulo adachoka ku
atene, nadza ku Korinto;
• Act 18:2 Ndipo adapeza Myuda wina dzina lake
Akula, fuko lake la ku Ponto, atachoka chatsopano
ku Italiya, pamodzi ndi mkazi wake Priskila,
(chifukwa cha Klaudiyo adalamulira Ayuda onse
achoke m’Roma;) ndipo Paulo adadza kwa iwo;
• Act 18:3 Ndipo popeza adali wa ntchito
imodzimodzi, adakhala nawo, ndipo iwowa
adagwira ntchito; pakuti ntchito yawo idali yosoka
mahema.
• Act 18:4 Ndipo adafotokozera m’sunagoge
masabata onse, nakopa Ayuda ndi Ahelene.
Chikhristu cha Pamwamba
The apostle (Paul) would also give an example
to the Christian ministry, dignifying and
honoring industry. While thus preaching and
working, he presented the highest type of
Christianity. He combined teaching with his
labor; and while toiling with those of his trade,
he instructed them concerning the way of
salvation. In pursuing this course, he had access
to many whom he could not otherwise have
reached. {LP 101.1}
Melrose, New England
We hope that those in charge of the work in New England will co-operate with
the Melrose sanitarium managers in taking aggressive steps to do the work that
should be done in Boston. A hundred workers could be laboring to advantage in
different portions of the city, in varied lines of service. {SpTB13 12.3}
The terrible disasters that are befalling great cities, ought to arouse us to
intense activity in giving the warning message to the people in these congested
centers of population, while we still have an opportunity. The most favorable
time for the presentation of our message in the cities, has passed by. Sin and
wickedness are rapidly increasing; and now we shall have to redeem the time
by laboring all the more earnestly. {SpTB13 13.1}
The medical missionary work is a door through which the truth is to find
entrance to many homes in the cities. In every city will be found those who will
appreciate the truths of the third angel's message. The judgments of God are
impending. Why do we not awaken to the peril threatening the men and
women living in the great cities of America? Our people do not realize as keenly
as they should the responsibility resting upon them to proclaim the truth to the
millions dwelling in these unwarned cities. {SpTB13 13.2} May 15, 1906.
Centres of Influence
GOSPEL IN PRACTICE
NYALI YANU IWALIRE